Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 55:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mawu a pakamwa pake ndi osalala ngati mafuta a mkaka,+

      Koma mtima wake umakonda ndewu.+

      Mawu ake ndi osalala ngati mafuta,+

      Koma ali ngati lupanga lakuthwa.+

  • Miyambo 26:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Munthu wodana nawe amadzibisa ndi milomo yake, koma mkati mwake mumakhala chinyengo.+

  • Mika 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anthu okhulupirika atha padziko lapansi, ndipo pakati pa anthu palibe munthu wowongoka mtima.+ Onse amadikirira anzawo kuti akhetse magazi.+ Aliyense amasaka m’bale wake ndi ukonde.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena