-
Mateyu 26:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Poyankha, Yudasi amene anali atatsala pang’ono kumupereka anati: “Nanga n’kukhala ine Rabi?” Iye anati: “Wanena wekha.”
-