1 Samueli 18:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tsiku lotsatira,+ mzimu woipa wochokera kwa Mulungu unayamba kugwira ntchito pa Sauli,+ moti anayamba kuchita zinthu ngati mneneri+ m’nyumba mwake. Pa nthawiyi, Davide anali kuimba nyimbo+ ngati kale ndipo Sauli anali ndi mkondo m’manja mwake.+ 1 Samueli 19:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndiyeno mzimu woipa wa Yehova+ unayamba kugwira ntchito pa Sauli ali m’nyumba mwake, atatenga mkondo m’manja mwake. Pa nthawiyi, Davide anali kumuimbira nyimbo. 1 Samueli 22:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndiyeno Sauli anamva kuti Davide ndi anthu amene anali naye apezeka. Iye anamva zimenezi ali ku Gibeya pamalo okwezeka, atakhala pansi pa mtengo wa bwemba.+ Sauliyo anali atagwira mkondo+ m’manja mwake ndipo atumiki ake onse anali atamuzungulira. 1 Samueli 26:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Chotero Davide anatenga mkondo ndi mtsuko wa madzi zimene zinali chakumutu kwa Sauli n’kunyamuka. Palibe munthu anawaona+ kapena kuzindikira kalikonse kapenanso kudzuka, pakuti onse anali m’tulo. Tulo timene anagonato tinali tulo tofa nato,+ tochokera kwa Yehova.
10 Tsiku lotsatira,+ mzimu woipa wochokera kwa Mulungu unayamba kugwira ntchito pa Sauli,+ moti anayamba kuchita zinthu ngati mneneri+ m’nyumba mwake. Pa nthawiyi, Davide anali kuimba nyimbo+ ngati kale ndipo Sauli anali ndi mkondo m’manja mwake.+
9 Ndiyeno mzimu woipa wa Yehova+ unayamba kugwira ntchito pa Sauli ali m’nyumba mwake, atatenga mkondo m’manja mwake. Pa nthawiyi, Davide anali kumuimbira nyimbo.
6 Ndiyeno Sauli anamva kuti Davide ndi anthu amene anali naye apezeka. Iye anamva zimenezi ali ku Gibeya pamalo okwezeka, atakhala pansi pa mtengo wa bwemba.+ Sauliyo anali atagwira mkondo+ m’manja mwake ndipo atumiki ake onse anali atamuzungulira.
12 Chotero Davide anatenga mkondo ndi mtsuko wa madzi zimene zinali chakumutu kwa Sauli n’kunyamuka. Palibe munthu anawaona+ kapena kuzindikira kalikonse kapenanso kudzuka, pakuti onse anali m’tulo. Tulo timene anagonato tinali tulo tofa nato,+ tochokera kwa Yehova.