Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pakuti Yehova amakonda chilungamo,+

      Ndipo sadzasiya anthu ake okhulupirika.+

      ע [ʽAʹyin]

      Adzawateteza mpaka kalekale.+

      Koma ana a anthu oipa adzaphedwa.+

  • Salimo 86:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Tetezani moyo wanga pakuti ndine wokhulupirika.+

      Inu ndinu Mulungu wanga, pulumutsani mtumiki wanu amene amakukhulupirirani.+

  • Salimo 97:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu okonda Yehova+ danani nacho choipa.+

      Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+

      Amawalanditsa m’manja mwa anthu oipa.+

  • Yeremiya 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pita, ndipo ukalengeze mawu awa kumpoto+ kuti:

      “‘Yehova wanena kuti: “Bwerera Isiraeli wopanduka iwe. Sindidzakuyang’anani mokwiya anthu inu+ pakuti ndine wokhulupirika,”+ watero Yehova.+ “Sindidzakhala wokwiya mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena