Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pakuti thanthwe lawo silofanana ndi Thanthwe lathu,+

      Ndipo adani athu angavomereze zimenezi.+

  • 1 Samueli 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Palibe woyera ngati Yehova. Palibe aliyense koma inu nokha.+

      Palibe thanthwe lofanana ndi Mulungu wathu.+

  • Salimo 18:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kodi pali Mulungu winanso woposa Yehova?+

      Kodi pali thanthwe linanso loposa Mulungu wathu?+

  • Salimo 94:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma Yehova adzakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+

      Ndipo Mulungu wanga adzakhala thanthwe langa lothawirako.+

  • Salimo 95:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 95 Bwerani tifuule kwa Yehova mokondwera!+

      Iye amene ndi Thanthwe la chipulumutso chathu, timufuulire mosangalala chifukwa wapambana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena