2 Samueli 5:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Kuyambira kale+ pamene Sauli anali mfumu yathu, inuyo munali kutsogolera Isiraeli polowa ndi potuluka.+ Ndipo Yehova anakuuzani kuti, ‘Udzaweta+ anthu anga Aisiraeli ndipo udzakhala mtsogoleri+ wa Isiraeli.’” 1 Mbiri 11:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Kuyambira kale, ngakhale pamene Sauli anali mfumu, inuyo munali kutsogolera Isiraeli polowa ndi potuluka.+ Ndipo Yehova Mulungu wanu anakuuzani kuti, ‘Udzaweta+ anthu anga Aisiraeli, ndipo udzakhala mtsogoleri+ wa anthu anga Aisiraeli.’”
2 Kuyambira kale+ pamene Sauli anali mfumu yathu, inuyo munali kutsogolera Isiraeli polowa ndi potuluka.+ Ndipo Yehova anakuuzani kuti, ‘Udzaweta+ anthu anga Aisiraeli ndipo udzakhala mtsogoleri+ wa Isiraeli.’”
2 Kuyambira kale, ngakhale pamene Sauli anali mfumu, inuyo munali kutsogolera Isiraeli polowa ndi potuluka.+ Ndipo Yehova Mulungu wanu anakuuzani kuti, ‘Udzaweta+ anthu anga Aisiraeli, ndipo udzakhala mtsogoleri+ wa anthu anga Aisiraeli.’”