Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Monga momwe Yehova anakhalira ndi inu mbuyanga mfumu,+ akhalenso ndi Solomo+ ndipo achititse mpando wake wachifumu kukhala waukulu+ kuposa mpando wanu wachifumu, mbuyanga Mfumu Davide.”

  • 1 Mbiri 28:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Akamatsatira malamulo anga+ ndi zigamulo zanga+ ndi mtima wonse ngati mmene akuchitira lero, ine ndidzakhazikitsa ufumu wake+ ndipo sudzagwedezeka mpaka kalekale.’

  • Salimo 89:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 ‘Ndidzakhazikitsa mbewu yako mpaka kalekale,+

      Ndipo ndidzalimbitsa mpando wako wachifumu+ ku mibadwomibadwo.’” [Seʹlah.]

  • Salimo 89:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Mbewu yake idzakhala mpaka kalekale,+

      Ndipo mpando wake wachifumu udzakhala ngati dzuwa pamaso panga.+

  • Luka 1:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Iye adzalamulira monga mfumu panyumba ya Yakobo kwamuyaya, moti ufumu wake sudzatha konse.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena