1 Samueli 17:50 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 50 Choncho Davide, mwa kugwiritsa ntchito gulaye ndi mwala, anali wamphamvu kuposa Mfilisiti. Iye anamukantha ndi kumupha, ndipo m’manja mwa Davide munalibe lupanga.+ 1 Samueli 18:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Akazi amene anali kusangalalawo anali kuimba molandizana mawu kuti:“Sauli wakantha adani ake masauzande,Ndipo Davide wakantha masauzande makumimakumi.”+ 1 Samueli 19:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Patapita nthawi, nkhondo inayambanso ndi Afilisiti. Davide anapita kukamenya nkhondoyo ndipo anakantha ndi kupha Afilisiti ochuluka,+ moti Afilisitiwo anathawa pamaso pake.+ 2 Samueli 10:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Asiriyawo anathawa+ pamaso pa Isiraeli, ndipo Davide anapha asilikali a Siriya 700 okwera magaleta,+ ndi asilikali 40,000 okwera pamahatchi. Iye anakanthanso Sobaki, mtsogoleri wa gulu lankhondo la Siriya, moti anafera pomwepo.+
50 Choncho Davide, mwa kugwiritsa ntchito gulaye ndi mwala, anali wamphamvu kuposa Mfilisiti. Iye anamukantha ndi kumupha, ndipo m’manja mwa Davide munalibe lupanga.+
7 Akazi amene anali kusangalalawo anali kuimba molandizana mawu kuti:“Sauli wakantha adani ake masauzande,Ndipo Davide wakantha masauzande makumimakumi.”+
8 Patapita nthawi, nkhondo inayambanso ndi Afilisiti. Davide anapita kukamenya nkhondoyo ndipo anakantha ndi kupha Afilisiti ochuluka,+ moti Afilisitiwo anathawa pamaso pake.+
18 Asiriyawo anathawa+ pamaso pa Isiraeli, ndipo Davide anapha asilikali a Siriya 700 okwera magaleta,+ ndi asilikali 40,000 okwera pamahatchi. Iye anakanthanso Sobaki, mtsogoleri wa gulu lankhondo la Siriya, moti anafera pomwepo.+