Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pamenepo Yehu anakoka uta+ wake n’kulasa Yehoramu kumsana pakati pamapewa, mpaka muviwo unatulukira pamtima pake, moti Yehoramu anagwa m’galeta lake lankhondo.+

  • 2 Mafumu 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pamenepo Yehu anawalemberanso kalata yachiwiri kuti: “Ngati muli kumbali yanga+ ndipo ngati muzimvera mawu anga, dulani mitu ya ana aamuna+ a mbuye wanu, ndipo mawa nthawi ngati yomwe ino mubwere nayo kwa ine ku Yezereeli.”+

      Ana aamuna a mfumuwo, omwe analipo 70, anali ndi akuluakulu a mumzindawo omwe anali kuwasamalira.

  • 2 Mafumu 10:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yehu atangomaliza kupereka nsembe yopserezayo, nthawi yomweyo anauza asilikali ake othamanga ndi othandiza pamagaleta kuti: “Lowani, apheni! Pasapezeke ndi mmodzi yemwe wotuluka panja.”+ Atamva zimenezi, asilikali ake othamanga ndi othandiza pamagaleta+ aja anayamba kupha anthuwo ndi lupanga n’kumaponyera mitembo yawo panja. Anakafika mpaka m’chipinda chamkati mwa kachisiyo chotchedwa mzinda wa Baala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena