Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Malire a gawo lawo anakafika ku Yezereeli,+ Kesulotu, Sunemu,+

  • 1 Mafumu 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno panali munda wa mpesa wa Naboti Myezereeli, umene unali ku Yezereeli,+ pafupi ndi nyumba yachifumu ya Ahabu mfumu ya Samariya.

  • 2 Mbiri 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho Yehoramu anabwerera n’kupita ku Yezereeli+ kuti akachire zilonda zimene anam’vulaza ku Rama,+ pamene anali kumenyana ndi Hazaeli mfumu ya Siriya.

      Chotero Azariya*+ mwana wa Yehoramu+ mfumu ya Yuda anapita ku Yezereeli kukaona Yehoramu+ mwana wa Ahabu chifukwa anali kudwala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena