Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ahaziya anayamba kulamulira ali ndi zaka 22 ndipo analamulira ku Yerusalemu chaka chimodzi.+ Mayi ake dzina lawo linali Ataliya+ mdzukulu wa Omuri+ mfumu ya Isiraeli.

  • 2 Mafumu 11:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu onse a m’dzikolo anapitiriza kusangalala,+ ndipo mumzindawo munali bata. Ataliya anali atamupha ndi lupanga panyumba ya mfumu.+

  • 2 Mbiri 21:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye anayenda m’njira ya mafumu a Isiraeli+ monga mmene ankachitira a m’nyumba ya Ahabu, chifukwa anakwatira mwana wa Ahabu.+ Ndipo iye anapitiriza kuchita zoipa pamaso pa Yehova.+

  • 2 Mbiri 22:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Ataliya,+ mayi wa Ahaziya ataona kuti mwana wake wafa, anapha ana onse achifumu a nyumba ya Yuda.+

  • 2 Mbiri 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pajatu ana+ a Ataliya mkazi woipa uja anathyola nyumba ya Mulungu woona,+ n’kutenga zinthu zonse zopatulika+ za m’nyumba ya Yehovayo n’kukazipereka kwa Abaala.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena