Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho amunawo anapita kukazonda dzikolo, kuyambira kuchipululu cha Zini+ mpaka ku Rehobu,+ kufupi ndi Hamati.+

  • Numeri 34:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kuchokera kuphiri la Hora, mukalembe malirewo akafike ku Hamati,+ mpaka ku Zedadi.+

  • Ezekieli 47:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ku Hamati,+ ku Berota,+ ku Siburaimu kumene ndi kumalire a Damasiko+ ndi Hamati. Malirewo akafikenso ku Hazere-hatikoni kufupi ndi malire a Haurani.+

  • Amosi 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano Yehova, Mulungu wa makamu wanena kuti, ‘Inu a m’nyumba ya Isiraeli, ine ndikukudzutsirani mtundu wa anthu+ umene udzakuponderezani kuyambira kumalire ndi Hamati+ mpaka kuchigwa cha Araba.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena