Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno Yehova anauza Gidiyoni kuti: “Ndidzapulumutsa anthu inu pogwiritsa ntchito amuna 300 amene anamwa madzi ndi manja awo, ndipo ndidzapereka Amidiyani m’manja mwanu.+ Koma ena onsewa, aliyense abwerere kwawo.”

  • 1 Samueli 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho Yonatani anauza mtumiki wake womunyamulira zida uja kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa amuna osadulidwawa.+ Pakuti mwina Yehova adzatithandiza, chifukwa palibe chimene chingalepheretse Yehova kupulumutsa anthu ake pogwiritsa ntchito anthu ambiri kapena ochepa.”+

  • Amosi 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iye ndiye amabweretsa chiwonongeko mwamsanga pa munthu wamphamvu ngati kuwala kwa mphezi. Ndiponso amachititsa kuti malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri awonongedwe.

  • 1 Akorinto 1:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma Mulungu anasankha zopusa za dziko+ kuti achititse manyazi anthu anzeru, ndipo Mulungu anasankha zinthu zofooka za dziko kuti achititse manyazi+ zinthu zamphamvu.

  • 2 Akorinto 12:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 koma anandiuza motsimikiza kuti: “Kukoma mtima kwakukulu kumene ndakusonyeza n’kokukwanira,+ pakuti mphamvu yanga imakhala yokwanira iweyo ukakhala wofooka.”+ Choncho, ndidzadzitamandira mosangalala kwambiri pa kufooka kwanga,+ kuti mphamvu ya Khristu ikhalebe pamutu panga ngati hema.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena