-
Amosi 5:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Iye ndiye amabweretsa chiwonongeko mwamsanga pa munthu wamphamvu ngati kuwala kwa mphezi. Ndiponso amachititsa kuti malo okhala ndi mpanda wolimba kwambiri awonongedwe.
-