1 Mbiri 9:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Alonda a pazipata+ anali Salumu,+ Akubu, Talimoni, ndi Ahimani. Salumu m’bale wawo ndiye anali mtsogoleri. Ezara 2:42 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 42 Ana a alonda a pachipata, omwe anali ana a Salumu,+ ana a Ateri,+ ana a Talimoni,+ ana a Akubu,+ ana a Hatita,+ ndi ana a Sobai, onse analipo 139. Nehemiya 7:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 Alonda a pachipata,+ ana a Salumu,+ ana a Ateri, ana a Talimoni,+ ana a Akubu,+ ana a Hatita, ana a Sobai,+ 138. Nehemiya 11:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Alonda a pazipata+ anali Akubu, Talimoni,+ ndi abale awo amene anali kulondera m’zipata.+ Onse pamodzi analipo 172.
17 Alonda a pazipata+ anali Salumu,+ Akubu, Talimoni, ndi Ahimani. Salumu m’bale wawo ndiye anali mtsogoleri.
42 Ana a alonda a pachipata, omwe anali ana a Salumu,+ ana a Ateri,+ ana a Talimoni,+ ana a Akubu,+ ana a Hatita,+ ndi ana a Sobai, onse analipo 139.
45 Alonda a pachipata,+ ana a Salumu,+ ana a Ateri, ana a Talimoni,+ ana a Akubu,+ ana a Hatita, ana a Sobai,+ 138.
19 Alonda a pazipata+ anali Akubu, Talimoni,+ ndi abale awo amene anali kulondera m’zipata.+ Onse pamodzi analipo 172.