Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Anthu odzichepetsa mudzawapulumutsa.+

      Koma mumatsutsa odzikweza, kuti muwatsitse.+

  • Salimo 18:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Chifukwa anthu osautsika mudzawapulumutsa,+

      Koma anthu odzikweza mudzawatsitsa.+

  • Miyambo 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yehova adzagwetsa nyumba za anthu odzikuza,+ koma adzakhazikitsa malire a malo a mkazi wamasiye.+

  • Yesaya 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Maso odzikuza a munthu wochokera kufumbi adzatsika, ndipo anthu odzikweza adzawerama.+ Yehova yekha ndi amene adzakwezedwe pamwamba m’tsiku limenelo.+

  • Danieli 4:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 “Tsopano ine Nebukadinezara ndikutamanda, kukweza ndi kulemekeza Mfumu yakumwamba,+ chifukwa ntchito zake zonse ndizo choonadi, njira zake ndi zolungama,+ ndiponso amatha kutsitsa anthu onyada.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena