Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Poona kuti sakuthanso kum’bisa,+ anatenga kabokosi kagumbwa* n’kukamata phula.+ Kenako anaikamo mwanayo n’kukasiya kabokosiko pakati pa mabango+ m’mphepete mwa mtsinje wa Nailo.

  • Yesaya 18:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Limeneli ndi dziko lomwe limatumiza nthumwi zake+ panyanja, m’ngalawa zoyenda pamadzi zopangidwa ndi gumbwa.* Limauza nthumwizo kuti: “Inu amithenga achangu, pitani ku mtundu wa anthu ataliatali osalala, anthu oopedwa ndi mitundu yonse ya anthu. Umenewu ndi mtundu wa anthu amphamvu kwambiri, ndiponso wopambana pa nkhondo, umene nthaka yake yakokoloka ndi mitsinje.”+

  • Yesaya 35:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Malo ouma chifukwa cha kutentha adzakhala dambo la madzi, ndipo malo aludzu adzakhala malo a akasupe amadzi.+ Kumalo okhala mimbulu,+ malo ake ousako, kudzakhala udzu wobiriwira, mabango ndi gumbwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena