Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Zitatero, Isaki anayamba kubzala mbewu m’dzikomo.+ M’chaka chimenechi anakolola zochuluka moti pa mbewu zimene anabzala, anakolola zochuluka kuwirikiza nthawi 100,+ popeza Yehova anali kum’dalitsa.+

  • Deuteronomo 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Madalitso onsewa adzakutsata ndi kukupeza+ chifukwa ukumvera mawu a Yehova Mulungu wako:

  • Salimo 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti inu Yehova mudzadalitsa aliyense wolungama.+

      Mudzamutchinga ndi chivomerezo chanu+ ngati kuti mukum’teteza ndi chishango chachikulu.+

  • Salimo 84:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti Yehova Mulungu ndi dzuwa+ ndiponso chishango.+

      Iye amatikomera mtima ndi kutipatsa ulemerero.+

      Yehova samana anthu oyenda mosalakwa chinthu chilichonse chabwino.+

  • Salimo 128:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti udzadya zipatso za ntchito ya manja ako.+

      Udzakhala wodala ndipo zinthu zidzakuyendera bwino.+

  • Miyambo 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Madalitso a Yehova ndi amene amalemeretsa,+ ndipo sawonjezerapo ululu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena