Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndi mmene zilili njira za onse oiwala Mulungu,+

      Ndipo chiyembekezo cha wampatuko chidzatha.+

  • Yobu 27:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kodi chiyembekezo cha wampatuko n’chiyani Mulungu akachotsa moyo wake,+

      Akamulanda moyo wake?+

  • Yobu 36:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Anthu ampatuko adzaunjika mkwiyo.+

      Iwo sadzalirira thandizo chifukwa chakuti iye wawamanga.

  • Salimo 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndani angakwere m’phiri la Yehova?+

      Ndipo ndani anganyamuke kukalowa m’malo ake opatulika?+

  • Yesaya 33:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mu Ziyoni, anthu ochimwa akuchita mantha.+ Opanduka akunjenjemera kwambiri.+ Akufunsa kuti: ‘Ndani wa ife angakhale pambali pa moto wowononga?+ Ndani wa ife angakhale pafupi ndi moto woyaka kwambiri wosatherapo?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena