Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndalefuka chifukwa cha kuusa moyo* kwanga.+

      Usiku wonse ndimanyowetsa bedi langa.+

      Ndimakhathamitsa bedi langa ndi misozi.+

  • Salimo 31:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndikomereni mtima inu Yehova, pakuti ndasautsika kwambiri.+

      Diso langa lafooka chifukwa cha chisoni,+ chimodzimodzinso moyo wanga ndi m’mimba mwanga.+

  • Maliro 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndikulirira zinthu zimenezi ngati mkazi.+ Maso anga ine! Maso anga akutuluka misozi.+

      Pakuti wonditonthoza, munthu woti anditsitsimule, ali kutali ndi ine.

      Ana anga asiyidwa+ popanda thandizo, pakuti mdani wanga wadzitukumula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena