Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ‘Yehova ndi wosakwiya msanga,+ ndipo ndi wodzaza ndi kukoma mtima kosatha.+ Amakhululukira wolakwa ndi wophwanya malamulo,+ koma iye salekerera konse wolakwa osam’langa.+ Amalanga ana, zidzukulu, ndi ana a zidzukuluzo chifukwa cha zolakwa za makolo awo.’+

  • Salimo 25:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Musakumbukire machimo a pa unyamata wanga ndi zolakwa zanga.+

      Ndikumbukireni malinga ndi kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Ndiponso chifukwa cha ubwino wanu, inu Yehova.+

  • Salimo 32:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zopweteka za woipa ndi zambiri.

      Koma wokhulupirira Yehova+ amazunguliridwa ndi kukoma mtima kosatha.+

  • Salimo 41:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma ine ndinati: “Inu Yehova, ndikomereni mtima.+

      Ndichiritseni, pakuti ndakuchimwirani.”+

  • Salimo 90:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 M’mawa mutikhutiritse ndi kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Kuti tifuule mokondwera ndi kuti tikhale osangalala masiku onse a moyo wathu.+

  • Salimo 103:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti monga mmene kumwamba kulili pamwamba kwambiri kuposa dziko lapansi,+

      Kukoma mtima kwake kosatha nakonso ndi kwapamwamba kwa onse omuopa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena