-
Salimo 104:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
104 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.+
Inu Yehova Mulungu wanga, mwasonyeza kuti ndinu wamkulu koposa.+
Mwadziveka ulemu ndi ulemerero.+
-