Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ulemu ndi ulemerero zili pamaso pake,+

      Pokhala pake pali mphamvu ndi chimwemwe.+

  • Yobu 37:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kunyezimira ngati kwa golide kumachokera kumpoto.

      Ulemu+ wa Mulungu ndi wochititsa mantha.

  • Salimo 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Inu Yehova Ambuye wathu, dzina lanu ndi lalikulu padziko lonse lapansi,+

      Inuyo ulemerero wanu ukusimbidwa kumwambamwamba!+

  • Salimo 96:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ulemu ndi ulemerero zili pamaso pake.+

      Mphamvu ndi kukongola zili m’nyumba yake yopatulika.+

  • Ezekieli 1:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Panali chinachake chooneka ngati utawaleza+ umene umaoneka mumtambo pa tsiku la mvula yamphamvu. Umu ndi mmene kuwala kozungulira pamalopo kunali kuonekera. Zinali kuoneka ngati ulemerero wa Yehova.+ Nditaona zimenezo, ndinagwada n’kuwerama mpaka nkhope yanga pansi.+ Kenako ndinayamba kumva mawu a winawake akulankhula.

  • Danieli 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Ndiyeno ndinapitiriza kuyang’ana kufikira pamene mipando yachifumu inaikidwa+ ndipo Wamasiku Ambiri+ anakhala pa mpando wake wachifumu. Zovala zake zinali zoyera kwambiri.+ Tsitsi lake linali looneka ngati ubweya wa nkhosa woyera.+ Mpando wake wachifumu unali kuyaka moto walawilawi,+ ndipo mawilo a mpandowo anali kuyaka moto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena