Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chifukwa cha kutukumuka mtima kwake, woipa safufuza kuti adziwe Mulungu.+

      Iye amangoganiza kuti: “Kulibe Mulungu.”+

  • Salimo 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Wopusa amanena mumtima mwake kuti:

      “Kulibe Yehova.”+

      Anthu oterewa amachita zoipa,+ ndipo amachita zinthu zonyansa.

      Palibe amene akuchita zabwino.+

  • Salimo 92:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Munthu wopanda nzeru sangadziwe zimenezi,+

      Ndipo munthu wopusa sangazimvetse.+

  • Aroma 1:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa chakuti, ngakhale anam’dziwa Mulungu, iwo sanam’patse ulemerero monga Mulungu kapena kumuyamikira.+ M’malomwake anayamba kulingalira zinthu zopanda pake+ ndipo mtima wawo wopusawo unachita mdima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena