Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Sisakiyo analanda mizinda ya Yuda+ yomwe inali ndi mipanda yolimba kwambiri, ndipo pamapeto pake anafika ku Yerusalemu.+

  • Yeremiya 52:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako gulu lonse lankhondo la Akasidi, lomwe linali ndi mkulu wa asilikali olondera mfumu uja, linagwetsa mpanda wonse wa Yerusalemu.+

  • Maliro 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova wameza malo okhala a Yakobo. Sanamvere chisoni malo ake alionse.+

      Mu ukali wake, iye wagwetsa mipanda yolimba kwambiri+ ya mwana wamkazi wa Yuda.

      Waipitsa ufumu+ ndi akalonga+ ake ndipo wawagwetsera pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena