Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Utsi unatuluka m’mphuno mwake, ndipo moto wotuluka m’kamwa mwake unanyeketsa.+

      Makala onyeka anatuluka mwa iye.

  • Salimo 50:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mulungu wathu adzabwera ndipo sadzakhala chete.+

      Pamaso pake pali moto wonyeketsa,+

      Ndipo pamalo onse omuzungulira pali mkuntho wamphamvu.+

  • Danieli 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mtsinje wa moto unali kuyenda kuchokera kwa iye.+ Panali atumiki okwana miliyoni imodzi amene anali kumutumikira nthawi zonse,+ ndi atumiki enanso mamiliyoni 100 amene anali kuimirira pamaso pake nthawi zonse.+ Bwalo la milandu+ linakhala pansi, ndipo mabuku anatsegulidwa.

  • Nahumu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye atapsa mtima, ndani angaime pamaso pake?+ Iye atakwiya, ndani angalimbe mtima kuima pamaso pake?+

      Mkwiyo wake adzaukhuthula ngati moto+ ndipo miyala idzagwetsedwa chifukwa cha iye.

  • Habakuku 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mliri unali kuyenda patsogolo pake+ ndipo matenda otenthetsa thupi anali kuyenda patsogolo pa mapazi ake.+

  • Aheberi 12:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Pakuti Mulungu wathu alinso moto wowononga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena