Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 79:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Musatiimbe mlandu chifukwa cha zolakwa za makolo athu.+

      Fulumirani! Tisonyezeni chifundo chanu,+

      Chifukwa tasautsika koopsa.+

  • Salimo 106:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Nthawi zambiri anali kuwalanditsa,+

      Koma iwo anali kumupandukira chifukwa sanali kumumvera,+

      Ndipo anali kuwatsitsa chifukwa cha zolakwa zawo.+

  • Salimo 142:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mvetserani kulira kwanga kochonderera,+

      Pakuti ndasautsika koopsa.+

      Ndipulumutseni kwa anthu amene akundizunza,+

      Pakuti iwo ndi amphamvu kuposa ine.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena