Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye wafukula dzenje, walikumbadi.+

      Koma adzagwera m’dzenje lokumba yekha.+

  • Salimo 35:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo andikumbira mbuna popanda chifukwa ndi kuikapo ukonde,+

      Akumba mbunazo kuti ndigweremo ngakhale kuti sindinalakwe.+

  • Salimo 119:78
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  78 Odzikuza achite manyazi, chifukwa andisocheretsa popanda chifukwa,+

      Koma ine ndimasinkhasinkha malamulo anu.+

  • Miyambo 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Munthu wopanda pake amafukula zinthu zoipa,+ ndipo pakamwa pake pamakhala mawu okhala ngati makala amoto.+

  • Yeremiya 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kodi zabwino amazibwezera ndi zoipa?+ Kumbukirani nthawi zonse zija pamene ndinaima pamaso panu kuwalankhulira zabwino kuti muwachotsere mkwiyo wanu.+ Koma iwo tsopano andikumbira mbuna.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena