Yesaya 44:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Ndine amene ndikuuza madzi akuya kuti, ‘Iphwa ndipo mitsinje yako yonse ndidzaiumitsa.’+ Yeremiya 50:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Madzi ake adzawonongedwa ndipo adzauma.+ Dziko limeneli ndi la zifaniziro zogoba,+ ndipo anthu ake amachita zinthu mosaganiza chifukwa cha masomphenya awo ochititsa mantha. Yeremiya 51:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 “Iwe mkazi wokhala pamadzi ambiri,+ wokhala ndi chuma chochuluka,+ mapeto ako afika ndipo nthawi yako+ yoti uzipanga phindu yatha.+ Yeremiya 51:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Akukanenanso kuti malo owolokera mtsinje alandidwa+ ndipo ngalawa zagumbwa* zatenthedwa. Amuna ankhondo nawonso asokonezeka.”+ Ezekieli 1:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 1 M’chaka cha 30, m’mwezi wachinayi, pa tsiku lachisanu la mweziwo, pamene ndinali pakati pa anthu amene anali ku ukapolo+ pafupi ndi mtsinje wa Kebara,+ kumwamba kunatseguka+ ndipo ndinayamba kuona masomphenya a Mulungu.+ Danieli 10:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndipo pa tsiku la 24 la mwezi woyamba, pamene ndinali m’mbali mwa mtsinje waukulu, mtsinje wa Hidekeli,+
38 Madzi ake adzawonongedwa ndipo adzauma.+ Dziko limeneli ndi la zifaniziro zogoba,+ ndipo anthu ake amachita zinthu mosaganiza chifukwa cha masomphenya awo ochititsa mantha.
13 “Iwe mkazi wokhala pamadzi ambiri,+ wokhala ndi chuma chochuluka,+ mapeto ako afika ndipo nthawi yako+ yoti uzipanga phindu yatha.+
32 Akukanenanso kuti malo owolokera mtsinje alandidwa+ ndipo ngalawa zagumbwa* zatenthedwa. Amuna ankhondo nawonso asokonezeka.”+
1 M’chaka cha 30, m’mwezi wachinayi, pa tsiku lachisanu la mweziwo, pamene ndinali pakati pa anthu amene anali ku ukapolo+ pafupi ndi mtsinje wa Kebara,+ kumwamba kunatseguka+ ndipo ndinayamba kuona masomphenya a Mulungu.+
4 Ndipo pa tsiku la 24 la mwezi woyamba, pamene ndinali m’mbali mwa mtsinje waukulu, mtsinje wa Hidekeli,+