Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 137:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 137 Tinakhala pansi+ m’mphepete mwa mitsinje ya ku Babulo,+

      Ndipo tinalira titakumbukira Ziyoni.+

  • Ezekieli 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Chotero ndinapita kwa anthu otengedwa ukapolo amene anali ku Tele-abibu, amene anali kukhala+ pafupi ndi mtsinje wa Kebara.+ Ndinayamba kukhala pamalo pamene anthuwo anali kukhala ndipo ndinakhala pamenepo masiku 7. Ndinangokhala phee pakati pawo, ndili m’maganizo.+

  • Ezekieli 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Akerubiwo anali zamoyo zomwe zija zimene ndinaziona kumtsinje wa Kebara.+ Akerubiwo akanyamuka kukwera m’mwamba,+

  • Ezekieli 43:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Zimene ndinaonazo zinali zofanana ndi zimene ndinaona m’masomphenya ena.+ Zinali zofanana ndi masomphenya amene ndinaona pamene ndinapita kukawononga mzinda.*+ Ndinaona zinthu zofanana ndi zimene ndinaona m’mphepete mwa mtsinje wa Kebara.+ Nditaona zimenezo, ndinagwada n’kuwerama mpaka nkhope yanga pansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena