Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Khalani wofunitsitsa kundilanditsa, inu Yehova.+

      Inu Yehova, fulumirani kundithandiza.+

  • Salimo 70:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Koma ine ndasautsika ndipo ndasauka.+

      Inu Mulungu, chitanipo kanthu mwamsanga kuti zinthu zindiyendere bwino.+

      Inu ndinu thandizo langa ndi Wopereka chipulumutso kwa ine.+

      Inu Yehova musachedwe.+

  • Salimo 71:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Mulungu, musakhale kutali ndi ine.+

      Inu Mulungu wanga, fulumirani kundithandiza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena