Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 22:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho Davide anachoka kumeneko+ ndi kuthawira+ kuphanga+ la Adulamu.+ Abale ake ndi nyumba yonse ya bambo ake anamva zimenezo, ndipo ananyamuka kumutsatira.

  • 1 Samueli 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Patapita nthawi, Sauli anafika kumakola a nkhosa amiyala m’mphepete mwa msewu, kumene kunali phanga. Choncho Sauli analowa mmenemo kukadzithandiza.+ Davide ndi amuna amene anali kuyenda naye anali atakhala pansi m’zigawo za mkatikati za phangalo,+ kumbuyo kwambiri.

  • Aheberi 11:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Iwo anali abwino kwambiri, osayenera kukhala m’dziko lotereli. Anayenda uku ndi uku m’zipululu, m’mapiri, m’mapanga,+ ndi m’maenje a dziko lapansi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena