Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 142:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Ndinachita zimenezi pamene mtima wanga+ unalefuka.

      Pamenepo, munadziwa njira yanga.+

      Adani anga anditchera msampha+

      M’njira imene ndikuyenda.+

  • 1 Akorinto 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma ngati munthu akukonda Mulungu,+ ameneyo amadziwika kwa Mulungu.+

  • Agalatiya 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma tsopano pamene mwadziwa Mulungu, kapena tinene kuti tsopano pamene mwadziwidwa ndi Mulungu,+ mukubwereranso bwanji ku mfundo zachibwanabwana,+ zomwe ndi zosathandiza ndiponso zopanda pake,+ n’kumafuna kukhalanso akapolo ake?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena