Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Wogwira ntchito ndi dzanja laulesi adzakhala wosauka,+ koma dzanja la munthu wakhama ndi limene limalemeretsa.+

  • Miyambo 23:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa chidakwa ndiponso munthu wosusuka adzasauka,+ ndipo kuwodzera kudzaveka munthu nsanza.+

  • Miyambo 27:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Munthu akakhuta amapondaponda uchi wa kuchisa, koma kwa munthu wanjala chinthu chilichonse chowawa chimatsekemera.+

  • 2 Atesalonika 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndiponso, pamene tinali ndi inu, tinali kukupatsani lamulo ili:+ “Ngati wina sakufuna kugwira ntchito, asadye.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena