Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho anapachika Hamani pamtengo+ umene anakonzera Moredekai,+ ndipo mkwiyo wa mfumu unatha.

  • Salimo 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iye wafukula dzenje, walikumbadi.+

      Koma adzagwera m’dzenje lokumba yekha.+

  • Salimo 10:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Modzikweza, woipa amathamangitsa wosautsika,+

      Ndipo wosautsikayo amakodwa ndi maganizo amene woipa walingalira.+

  • Miyambo 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Woipa amangofunafuna kupanduka,+ ndipo munthu amene watumidwa kuti akamulange sam’chitira chifundo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena