Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno anati: “Tiyeni timange mzinda wathuwathu, ndipo nsanja yake ikafike m’mwamba mwenimweni.+ Tikatero tidzipangira dzina loti titchuke nalo,+ ndipo sitibalalikana padziko lonse lapansi.”+

  • Salimo 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mavuto ake adzabwerera pamutu pake,+

      Ndipo chiwawa chake chidzatsikira paliwombo pake.+

  • Salimo 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti akuchitirani zinthu zoipa.+

      Alinganiza kuchita zinthu zimene sangazikwanitse.+

  • Salimo 37:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Khala chete pamaso pa Yehova,+

      Ndipo umuyembekezere ndi mtima wako wonse.+

      Usapse mtima ndi aliyense amene zinthu zikumuyendera bwino,+

      Munthu amene akukwaniritsa zolinga zake zoipa.+

  • Miyambo 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Woipa adzagwidwa ndi zolakwa zake zomwe,+ ndipo adzamangidwa m’zingwe za tchimo lake lomwe.+

  • Miyambo 26:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Amene akukumba dzenje adzagweramo yekha,+ ndipo amene akugubuduza mwala udzabwerera kwa iye.+

  • Chivumbulutso 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mafumuwa maganizo awo ndi amodzi, choncho adzapereka mphamvu zawo ndi ulamuliro wawo kwa chilombocho.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena