Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti akuchitirani zinthu zoipa.+

      Alinganiza kuchita zinthu zimene sangazikwanitse.+

  • Miyambo 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Munthu angaganize za njira zake mumtima mwake,+ koma Yehova ndiye amawongolera mayendedwe ake.+

  • Miyambo 19:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mumtima mwa munthu mumakhala zolinga zambiri,+ koma zolinga za Yehova n’zimene zidzakwaniritsidwe.+

  • Miyambo 20:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mayendedwe a mwamuna wamphamvu amachokera kwa Yehova,+ koma kodi munthu wochokera kufumbi angazindikire bwanji njira yake?+

  • 1 Akorinto 7:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Koma ngati wina ndi wokhazikika mumtima mwake ndipo alibe chomuvutitsa, koma amatha kulamulira mtima wake, ndipo wasankha mumtima mwake kukhalabe wosakwatira,* wachita bwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena