Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:67
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 67 Zitatero, Isaki analowa ndi mkaziyo m’hema wa Sara, mayi ake.+ Umu ndi mmene Isaki anatengera Rabeka kukhala mkazi wake.+ Iye anam’konda kwambiri,+ ndipo anatonthozedwa pambuyo pa imfa ya mayi ake.+

  • Miyambo 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mkazi wabwino ndi chisoti cha ulemu kwa mwamuna wake,*+ koma mkazi wochita zinthu zochititsa manyazi ali ngati chowoletsa mafupa a mwamunayo.+

  • Miyambo 31:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mkazi wabwino, ndani angam’peze?+ Mtengo wake umaposa wa miyala yamtengo wapatali.

  • Mlaliki 9:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Sangalala ndi moyo limodzi ndi mkazi wako amene umamukonda+ masiku onse a moyo wako wachabechabe, amene Mulungu wakupatsa padziko lapansi pano. Usangalale masiku ako onse achabechabe, pakuti imeneyo ndiyo mphoto yako pamoyo,+ ndi pa ntchito yovuta imene ukuigwira mwakhama padziko lapansi pano.

  • 1 Akorinto 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma chifukwa cha kuwanda kwa dama,*+ mwamuna aliyense akhale ndi mkazi wakewake+ ndipo mkazi aliyense akhale ndi mwamuna wakewake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena