Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Munthu akagwiritsitsa nzeru, zidzakhala ngati mtengo wa moyo+ kwa iye, ndipo ozigwiritsitsa+ adzatchedwa odala.+

  • Miyambo 8:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Pakuti wondipeza ine, ndithu adzapezanso moyo+ ndipo Yehova adzasangalala naye,+

  • Miyambo 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti ine ndidzachititsa kuti masiku ako akhale ambiri+ ndipo zaka za moyo wako zidzawonjezeredwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena