Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 11:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Kenako Solomo anagona pamodzi ndi makolo ake,+ ndipo anaikidwa m’manda mu Mzinda wa Davide+ bambo ake. Kenako mwana wake Rehobowamu,+ anayamba kulamulira m’malo mwake.

  • Salimo 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndipulumutseni kwa anthu ndi dzanja lanu, inu Yehova,+

      Ndipulumutseni kwa anthu a m’nthawi* ino,+ amene gawo lawo lili m’moyo uno.+

      Anthu amene mimba zawo mwazidzaza ndi chuma chanu chobisika,+

      Amene ali ndi ana aamuna ochuluka,+

      Ndipo amakundikira ana awo chuma.+

  • Salimo 39:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Zoonadi, munthu amayenda ngati chithunzithunzi.+

      Ndithudi, anthu amapokosera pachabe.+

      Munthu amaunjika zinthu ndipo sadziwa amene adzazitute.+

  • Luka 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Mulungu anamuuza kuti, ‘Wopanda nzeru iwe, usiku womwe uno moyo wako adzaufuna.+ Nanga chuma chimene waunjikachi chidzakhala cha ndani?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena