Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pakuti anthu oipa adzatheratu onse,+

      Ndipo adani a Yehova adzafanana ndi busa la msipu wobiriwira mochititsa kaso.

      Iwo adzatha.+ Adzazimiririka ndi kusanduka utsi.+

  • Hoseya 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ine ndidzakhala ngati mkango wamphamvu kwa Efuraimu+ ndiponso ngati mkango wamphongo kwa nyumba ya Yuda. Ineyo ndidzawakhadzulakhadzula ndekha ndi kuwataya ndipo sipadzakhala wowalanditsa.+

  • Mika 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Tamverani! Yehova akuchoka pamalo ake,+ ndipo atsika ndi kupondaponda m’malo okwezeka a padziko lapansi.+

  • Mateyu 24:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti pa nthawiyo kudzakhala chisautso chachikulu+ chimene sichinachitikepo kuchokera pa chiyambi cha dziko mpaka tsopano,+ ndipo sichidzachitikanso.

  • 2 Atesalonika 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pa nthawi imeneyo adzabwezera chilango+ kwa anthu osadziwa Mulungu+ ndi kwa anthu osamvera uthenga wabwino+ wonena za Ambuye wathu Yesu.+

  • 2 Petulo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndipo mwa mawu amodzimodziwo, kumwamba+ kumene kulipo panopa limodzi ndi dziko lapansi,+ azisungira moto+ m’tsiku lachiweruzo+ ndi chiwonongeko cha anthu osaopa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena