Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Mulungu anati: “N’chiyani chimene wachitachi? Tamvera tsono. Magazi a m’bale wako akundilirira munthaka.+

  • Salimo 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pofunafuna okhetsa magazi,+ iye adzakumbukira ndithu anthu osautsidwa.+

      Sadzaiwala ndithu kulira kwawo.+

  • Ezekieli 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakuti magazi amene mzindawo wakhetsa ali mkati mwake.+ Waika magaziwo pathanthwe losalala, pamalo oonekera. Mzindawo sunathire magaziwo pansi kuti uwakwirire ndi dothi.+

  • Luka 11:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 N’chifukwa chake m’badwo uwu udzafunsidwa za magazi a aneneri,+ okhetsedwa kuchokera pamene dziko linakhazikika.+

  • Chivumbulutso 16:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 pakuti iwo anakhetsa magazi a oyera ndi a aneneri.+ Ndipo inu mwawapatsa magazi+ kuti amwe, ndipo n’zowayenereradi.”+

  • Chivumbulutso 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mwa iye munapezeka magazi+ a aneneri,+ a oyera,+ ndi a onse amene anaphedwa padziko lapansi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena