Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Yehova andibwezere mogwirizana ndi chilungamo changa,+

      Andibwezere mogwirizana ndi kuyera kwa manja anga pamaso pake.+

  • Salimo 128:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 128 Wodala ndi aliyense woopa Yehova,+

      Amene amayenda m’njira za Mulungu.+

  • Mlaliki 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngakhale woipa atachita zoipa+ maulendo 100 n’kukhala ndi moyo wautali akuchitabe zofuna zake, ine ndikudziwa kuti anthu amene amaopa Mulungu woona zidzawayendera bwino,+ chifukwa chakuti anali kumuopa.+

  • Zefaniya 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 bwerani kwa Yehova,+ inu nonse ofatsa a padziko lapansi,+ amene mwakhala mukutsatira zigamulo zake. Yesetsani kukhala olungama,+ yesetsani kukhala ofatsa.+ Mwina+ mungadzabisike pa tsiku la mkwiyo wa Yehova.+

  • Aroma 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma aliyense wochita zabwino,+ choyamba Myuda+ kenako Mgiriki,+ adzalandira ulemerero, ulemu ndi mtendere.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena