Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pakuti Yehova amadziwa njira za olungama,+

      Koma oipa adzatheratu pamodzi ndi njira zawo.+

  • Salimo 37:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Koma anthu onse ochimwa adzafafanizidwa.+

      M’tsogolo, anthu oipa adzaphedwa.+

  • Salimo 104:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ochimwa adzafafanizidwa padziko lapansi.+

      Ndipo anthu oipa sadzakhalaponso.+

      Tamanda Yehova, iwe moyo wanga. Tamandani Ya, anthu inu!*+

  • Miyambo 29:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Munthu wodzudzulidwa kawirikawiri+ koma amene amaumitsa khosi lake,+ adzathyoledwa mwadzidzidzi ndipo akadzatero sadzachira.+

  • Ezekieli 20:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Ndidzachotsa pakati panu anthu ondipandukira ndi ondichimwira.+ Pakuti ndidzawatulutsa m’dziko limene akukhalamo monga alendo, koma sadzalowa m’dziko la Isiraeli,+ ndipo anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova.’+

  • 2 Petulo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndipo mwa mawu amodzimodziwo, kumwamba+ kumene kulipo panopa limodzi ndi dziko lapansi,+ azisungira moto+ m’tsiku lachiweruzo+ ndi chiwonongeko cha anthu osaopa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena