Salimo 49:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Mvetserani izi, anthu nonsenu.Tcherani khutu inu nonse a m’nthawi* ino,+ Miyambo 1:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Iyo imafuula kumapeto kwa misewu yaphokoso.+ Pazipata zolowera mumzinda, imanena mawu ake kuti:+ Yeremiya 19:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ukawauze kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova inu mafumu a Yuda ndi inu okhala mu Yerusalemu.+ Yehova wa makamu,+ Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “‘“Ine ndikubweretsa tsoka pamalo ano, ndipo aliyense akadzamva za tsoka limeneli, makutu ake adzalira.+ Yeremiya 22:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ukanene kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova, inu mfumu ya Yuda amene mwakhala pampando wachifumu wa Davide.+ Mumve mawu amenewa inuyo, atumiki anu komanso anthu anu amene amalowa pazipata izi.+
49 Mvetserani izi, anthu nonsenu.Tcherani khutu inu nonse a m’nthawi* ino,+ Miyambo 1:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Iyo imafuula kumapeto kwa misewu yaphokoso.+ Pazipata zolowera mumzinda, imanena mawu ake kuti:+ Yeremiya 19:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ukawauze kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova inu mafumu a Yuda ndi inu okhala mu Yerusalemu.+ Yehova wa makamu,+ Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “‘“Ine ndikubweretsa tsoka pamalo ano, ndipo aliyense akadzamva za tsoka limeneli, makutu ake adzalira.+ Yeremiya 22:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ukanene kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova, inu mfumu ya Yuda amene mwakhala pampando wachifumu wa Davide.+ Mumve mawu amenewa inuyo, atumiki anu komanso anthu anu amene amalowa pazipata izi.+
3 Ukawauze kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova inu mafumu a Yuda ndi inu okhala mu Yerusalemu.+ Yehova wa makamu,+ Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “‘“Ine ndikubweretsa tsoka pamalo ano, ndipo aliyense akadzamva za tsoka limeneli, makutu ake adzalira.+
2 Ukanene kuti, ‘Tamverani mawu a Yehova, inu mfumu ya Yuda amene mwakhala pampando wachifumu wa Davide.+ Mumve mawu amenewa inuyo, atumiki anu komanso anthu anu amene amalowa pazipata izi.+