-
Yeremiya 11:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Makolo anu ndinawalamula kumvera mawu amenewa pamene ndinali kuwatulutsa m’dziko la Iguputo,+ pamene ndinali kuwatulutsa m’ng’anjo yachitsulo.+ Ndinawalamula kuti, ‘Muzimvera mawu anga, ndipo muzichita zinthu motsatira malamulo onse amene ndakupatsani.+ Mukatero mudzakhaladi anthu anga, ndipo ine ndidzakhala Mulungu wanu,+
-