Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mapazi anga ayendebe m’njira zanu,+

      Mmene sadzapunthwa ngakhale pang’ono.+

  • Salimo 37:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova walimbitsa mapazi a munthu wamphamvu zake,+

      Ndipo Mulungu amakondwera ndi njira zake.+

  • Miyambo 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pereka ntchito zako kwa Yehova,+ ndipo zolinga zako ndithu zidzakhazikika.+

  • Miyambo 20:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mayendedwe a mwamuna wamphamvu amachokera kwa Yehova,+ koma kodi munthu wochokera kufumbi angazindikire bwanji njira yake?+

  • Yeremiya 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Mtima ndi wonyenga kwambiri kuposa china chilichonse ndipo ungathe kuchita china chilichonse choipa.*+ Ndani angaudziwe?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena