Yobu 12:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Mahema a anthu olanda amakhala opanda nkhawa,+Ndipo anthu okwiyitsa Mulungu amakhala pa mtendereWofanana ndi wa munthu amene watenga mulungu* m’manja mwake.+ Yobu 21:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 N’chifukwa chiyani oipa amakhalabe ndi moyo,+Amakalamba komanso amalemera kwambiri?+ Salimo 37:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 37 Usapse mtima chifukwa cha anthu ochita zoipa.+Usakhumbe kukhala ngati anthu ochita zosalungama.+ Salimo 73:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pakuti ndinachitira nsanje anthu odzitukumula,+Ndikamaona mtendere wa anthu oipa.+ Yeremiya 5:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Iwo anenepa+ ndipo matupi awo asalala. Achitanso zinthu zoipa zosawerengeka. Iwo sanaweruze mlandu wa munthu aliyense mwachilungamo,+ ngakhale mlandu wa mwana wamasiye,*+ pofuna kuti zinthu ziwayendere bwino.+ Iwo sanachitire chilungamo munthu wosauka.’” Malaki 3:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Panopa anthu odzikuza tikuwatcha odala.+ Komanso anthu ochita zoipa zinthu zikuwayendera bwino.+ Iwo ayesa Mulungu koma sakulandira chilango.’”+
6 Mahema a anthu olanda amakhala opanda nkhawa,+Ndipo anthu okwiyitsa Mulungu amakhala pa mtendereWofanana ndi wa munthu amene watenga mulungu* m’manja mwake.+
28 Iwo anenepa+ ndipo matupi awo asalala. Achitanso zinthu zoipa zosawerengeka. Iwo sanaweruze mlandu wa munthu aliyense mwachilungamo,+ ngakhale mlandu wa mwana wamasiye,*+ pofuna kuti zinthu ziwayendere bwino.+ Iwo sanachitire chilungamo munthu wosauka.’”
15 Panopa anthu odzikuza tikuwatcha odala.+ Komanso anthu ochita zoipa zinthu zikuwayendera bwino.+ Iwo ayesa Mulungu koma sakulandira chilango.’”+