Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mudzawabweretsa ndi kuwakhazikitsa m’phiri limene ndi cholowa chanu.+

      Malo okhazikika amene mwakonzeratu kuti mukakhalemo,+ inu Yehova.

      Malo opatulika+ amene manja anu, inu Yehova, anakhazikitsa.

  • Salimo 44:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Munapitikitsa anthu a mitundu ina ndi dzanja lanu,+

      Ndipo m’malo mwawo munakhazikitsa anthu anu.+

      Munagonjetsa mitundu ya anthu ndi kuipitikitsa.+

  • Salimo 80:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Munachititsa mtengo wa mpesa kuchoka mu Iguputo.+

      Munapitikitsa mitundu ya anthu kuti mubzalemo mtengowo.+

  • Yesaya 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndikufuna ndimuimbire nyimbo munthu amene ndimamukonda. Imeneyi ndi nyimbo yonena za munthu amene ndimamukonda, ndiponso munda wake wa mpesa.+ Wokondedwa wanga anali ndi munda wa mpesa pamalo achonde m’mbali mwa phiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena