Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 24:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mfumu ya Iguputo sinatulukenso+ m’dziko lake,+ chifukwa mfumu ya Babulo inali itatenga zinthu zonse zomwe zinali za mfumu ya Iguputo,+ kuyambira kuchigwa*+ cha Iguputo kukafika kumtsinje wa Firate.+

  • Yesaya 20:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iwo adzachita mantha ndiponso manyazi chifukwa chakuti anali kudalira Itiyopiya+ komanso chifukwa chakuti anali kusirira kukongola kwa Iguputo.+

  • Maliro 1:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndaitana anthu ondikonda kwambiri,+ koma anthuwo andichitira zachinyengo.

      Ansembe anga ndiponso akuluakulu atha+ mumzinda.

      Atha pamene anali kufunafuna chakudya choti adye kuti adzitsitsimutse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena