Salimo 48:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Phiri la Ziyoni limene lili m’dera lakutali la kumpoto,+Ndi lokongola chifukwa lili pamalo okwezeka ndi osangalatsa padziko lonse lapansi,+Mudzi wa Mfumu Yaikulu.+ Danieli 8:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Imodzi mwa nyangazi inatulutsa nyanga ina yaing’ono+ imene inayamba kukula kwambiri moloza kum’mwera, moloza kotulukira dzuwa ndiponso moloza ku Dziko Lokongola.+ Danieli 11:41 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 41 Iyo idzalowanso+ m’Dziko Lokongola+ ndipo idzachititsa mayiko ambiri kupunthwa,+ koma Edomu, Mowabu+ ndi mbali yaikulu ya ana a Amoni adzapulumuka m’manja mwake. Zekariya 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 ‘Chotero ndinawabalalitsira ku mitundu yonse ya anthu+ imene sanali kuidziwa,+ ngati kuti atengedwa ndi mphepo yamkuntho. Dzikoli analisiya labwinja, popanda munthu wodutsamo kapena kuyendayendamo.+ Iwo anasandutsa dziko losiririka+ kukhala chinthu chodabwitsa.’”
2 Phiri la Ziyoni limene lili m’dera lakutali la kumpoto,+Ndi lokongola chifukwa lili pamalo okwezeka ndi osangalatsa padziko lonse lapansi,+Mudzi wa Mfumu Yaikulu.+
9 Imodzi mwa nyangazi inatulutsa nyanga ina yaing’ono+ imene inayamba kukula kwambiri moloza kum’mwera, moloza kotulukira dzuwa ndiponso moloza ku Dziko Lokongola.+
41 Iyo idzalowanso+ m’Dziko Lokongola+ ndipo idzachititsa mayiko ambiri kupunthwa,+ koma Edomu, Mowabu+ ndi mbali yaikulu ya ana a Amoni adzapulumuka m’manja mwake.
14 ‘Chotero ndinawabalalitsira ku mitundu yonse ya anthu+ imene sanali kuidziwa,+ ngati kuti atengedwa ndi mphepo yamkuntho. Dzikoli analisiya labwinja, popanda munthu wodutsamo kapena kuyendayendamo.+ Iwo anasandutsa dziko losiririka+ kukhala chinthu chodabwitsa.’”